Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 38:2 - Buku Lopatulika

2 Pakuti mivi yanu yandilowa, ndi dzanja lanu landigwera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Pakuti mivi yanu yandilowa, ndi dzanja lanu landigwera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Mivi yanu yandilasa, ndipo dzanja lanu landipsinja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Pakuti mivi yanu yandilasa, ndipo dzanja lanu latsika ndipo landifikira.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 38:2
12 Mawu Ofanana  

Pakuti mivi ya Wamphamvuyonse yandilowa, mzimu wanga uwumwa ulembe wake; zoopsa za Mulungu zindindandira nkhondo.


Pakuti mudzawabweza m'mbuyo, popiringidza m'nsinga zanu pankhope pao.


Chifukwa usana ndi usiku dzanja lanu linandilemera ine; uwisi wanga unasandulika kuuma kwa malimwe.


Mundichitire chifundo, Yehova; pakuti ndalefuka ine. Mundichize, Yehova; pakuti anthunthumira mafupa anga.


Koma Mulungu adzawaponyera muvi; adzalaswa modzidzimutsa.


Wathifula uta wake, nandiyesa polozetsa muvi.


Komanso dzanja la Yehova linatsutsana nao, kuwaononga m'chigono, kufikira adawatha.


kodi mudzawalindirira akakula? Mudzadziletsa osakwatibwa? Iai, ana anga, pakuti chandiwawa koposa chifukwa cha inu popeza dzanja la Yehova landitulukira.


Chifukwa chake anatumiza, nasonkhanitsa mafumu onse a Afilisti, ndipo iwowa anati, Chotsani likasa la Mulungu wa Israele, lipitenso kumalo kwake, kuti lingationonge ife, ndi anthu athu; pakuti kunali kusautsa koopsa m'mzinda monse; dzanja la Mulungu linavutadi pamenepo.


Koma Yehova anavuta iwo a ku Asidodi ndi dzanja lake, nawaononga, nawazunza ndi mafundo, mu Asidodi ndi m'midzi yake.


Ndipo muyang'anire, ngati likwera panjira ya malire akeake ku Betesemesi, Iye anatichitira choipa ichi chachikulu; koma likapanda kutero, tidzadziwapo kuti dzanja limene linatikantha, silili lake; langotigwera tsokali.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa