Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 38:22 - Buku Lopatulika

22 Fulumirani kundithandiza, Ambuye, chipulumutso changa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Fulumirani kundithandiza, Ambuye, chipulumutso changa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Fulumirani kudzandithandiza, Inu Ambuye, Mpulumutsi wanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Bwerani msanga kudzandithandiza, Inu Ambuye Mpulumutsi wanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 38:22
11 Mawu Ofanana  

Yehova, ndaitana kwa Inu; ndifulumireni ine; munditcherere khutu, pamene ndiitana kwa Inu.


Ng'ombe zamphongo zambiri zandizinga; mphongo zolimba za ku Basani zandizungulira.


Yehova ndiye kuunika kwanga ndi chipulumutso changa; ndidzaopa yani? Yehova ndiye mphamvu ya moyo wanga; ndidzachita mantha ndi yani?


Ndikupemphani, Yehova, ndilanditseni; fulumirani kudzandithandiza, Yehova.


Ndipo ine ndine wozunzika ndi waumphawi; koma Ambuye andikumbukira ine. Inu ndinu mthandizi wanga, ndi Mpulumutsi wanga, musamachedwa, Mulungu wanga.


Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa; msanje wanga, sindidzagwedezeka kwakukulu.


Iye yekhayo ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa, msanje wanga, sindidzagwedezeka.


Fulumirani kundipulumutsa, Mulungu! Fulumirani kundithandiza, Yehova.


Koma ine ndine wozunzika ndi waumphawi; mundifulumirire, Mulungu. Inu ndinu mthandizi wanga ndi Mpulumutsi wanga; musachedwe, Yehova.


Musandikhalire kutali, Mulungu; fulumirani kundithandiza, Mulungu.


Taonani, Mulungu ndiye chipulumutso changa; ndidzakhulupirira, sindidzaopa; pakuti Yehova Mwini ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga, Iye ndiye chipulumutso changa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa