Masalimo 38:21 - Buku Lopatulika21 Musanditaye, Yehova, Mulungu wanga, musakhale kutali ndi ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Musanditaye, Yehova, Mulungu wanga, musakhale kutali ndi ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Musandisiye ndekha, Inu Chauta, Inu Mulungu wanga, musakhale nane kutali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Inu Yehova, musanditaye; musakhale kutali ndi ine Mulungu wanga. Onani mutuwo |