Masalimo 38:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo iwo akubwezera choipa pa chabwino atsutsana nane, popeza nditsata chabwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo iwo akubwezera choipa pa chabwino atsutsana nane, popeza nditsata chabwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Anthu amene amandibwezera zoipa m'malo mwa zabwino ndiwo adani anga, chifukwa ine ndimachita zabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iwo amene amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino amandinyoza pamene nditsatira zabwino. Onani mutuwo |