Masalimo 38:19 - Buku Lopatulika19 Koma adani anga ali ndi moyo, nakhala ndi mphamvu, ndipo akundida kopanda chifukwa achuluka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma adani anga ali ndi moyo, nakhala ndi mphamvu, ndipo akundida kopanda chifukwa achuluka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ngamphamvu adani amene amafuna moyo wanga, ngambiri amene amandida popanda chifukwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ambiri ndi adani anga amphamvu; amene amandida popanda chifukwa alipo ochuluka kwambiri. Onani mutuwo |