Masalimo 38:18 - Buku Lopatulika18 Pakuti ndidzafotokozera mphulupulu yanga; nditenga nkhawa chifukwa cha tchimo langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakuti ndidzafotokozera mphulupulu yanga; nditenga nkhawa chifukwa cha tchimo langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndikuvomera kuipa kwanga, ndikuda nkhaŵa chifukwa cha machimo anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndikuvomereza mphulupulu zanga; ndipo ndavutika ndi tchimo langa. Onani mutuwo |