Masalimo 38:17 - Buku Lopatulika17 Ndafikana potsimphina, ndipo chisoni changa chili pamaso panga chikhalire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndafikana potsimphina, ndipo chisoni changa chili pamaso panga chikhalire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Inde, ndili pafupi kugwa, ndipo ndikumva kuŵaŵa nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Pakuti ndili pafupi kugwa, ndipo ndikumva kuwawa nthawi zonse. Onani mutuwo |