Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 38:16 - Buku Lopatulika

16 Pakuti ndinati, Asakondwerere ine; pakuterereka phazi langa, asadzikuze pa ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Pakuti ndinati, Asakondwerere ine; pakuterereka phazi langa, asadzikuze pa ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Popeza ndimapemphera kuti, “Musalole konse kuti akondwerere pa ine, amene amandinyodola akaona kuti ndikuterereka.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere kapena kudzikweza okha pa ine pamene phazi langa laterereka.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 38:16
4 Mawu Ofanana  

Pamene ndinati, Literereka phazi langa, chifundo chanu, Yehova, chinandichirikiza.


Kubwezera chilango nkwanga, kubwezera komwe, pa nyengo ya kuterereka phazi lao; pakuti tsiku la tsoka lao layandika, ndi zinthu zowakonzeratu zifulumira kudza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa