Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 38:15 - Buku Lopatulika

15 Pakuti ndikuyembekezani Inu, Yehova; Inu mudzayankha, Ambuye Mulungu wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Pakuti ndikuyembekezani Inu, Yehova; Inu mudzayankha, Ambuye Mulungu wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Koma tsono ndimayembekezera Inu Chauta, Ndinu Chauta, Mulungu wanga amene mudzayankha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Ndikudikira Inu Yehova; mudzayankha, Inu Ambuye Mulungu wanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 38:15
5 Mawu Ofanana  

Tsiku loitana ine, munandiyankha, munandilimbitsa ndi mphamvu m'moyo mwanga.


Ine ndinakuitanani, pakuti mudzandiyankha, Mulungu; tcherani khutu lanu kwa ine, imvani mau anga.


Ndipo tsopano, Ambuye, ndilindira chiyani? Chiyembekezo changa chili pa Inu.


Iye anatsenderezedwa koma anadzichepetsa yekha osatsegula pakamwa pake; ngati nkhosa yotsogoleredwa kukaphedwa, ndi ngati mwanawankhosa amene ali duu pamaso pa omsenga, motero sanatsegule pakamwa pake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa