Masalimo 37:9 - Buku Lopatulika9 Pakuti ochita zoipa adzadulidwa; koma iwo akuyembekeza Yehova, iwowa adzalandira dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Pakuti ochita zoipa adzadulidwa; koma iwo akuyembekeza Yehova, iwowa adzalandira dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pajatu anthu oipa adzaonongeka, koma okhulupirira Chauta adzalandira dziko kuti likhale lao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pakuti anthu oyipa adzachotsedwa, koma iwo amene amayembekeza mwa Yehova adzalandira dziko. Onani mutuwo |