Masalimo 37:8 - Buku Lopatulika8 Leka kupsa mtima, nutaye mkwiyo; usavutike mtima ungachite choipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Leka kupsa mtima, nutaye mkwiyo; usavutike mtima ungachite choipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Lewa kupsa mtima ndi kukwiya. Usachite zimenezi, pakuti sudzapindula nazo kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Pewa kupsa mtima ndipo tembenuka kuchoka ku ukali, usavutike chifukwa zimenezi zimatsogolera ku zoyipa. Onani mutuwo |