Masalimo 37:10 - Buku Lopatulika10 Katsala kanthawi ndipo woipa adzatha psiti; inde, udzayang'anira mbuto yake, nudzapeza palibe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Katsala kanthawi ndipo woipa adzatha psiti; inde, udzayang'anira mbuto yake, nudzapeza palibe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Kanthaŵi pang'ono ndipo munthu woipa sadzakhalaponso, ngakhale muyang'ane bwino pamalo pamene analiri, simudzampezapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kwa kanthawi oyipa sadzapezekanso; ngakhale muwafunefune, sadzapezekanso. Onani mutuwo |