Masalimo 37:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo adzaonetsa chilungamo chako monga kuunika, ndi kuweruza kwako monga usana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo adzaonetsa chilungamo chako monga kuunika, ndi kuweruza kwako monga usana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Adzaonetsa poyera kusalakwa kwako, ndipo kulungama kwako kudzaŵala ngati usana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iye adzachititsa chilungamo chako kuwala ngati mʼbandakucha, chiweruzo chako ngati dzuwa la masana. Onani mutuwo |