Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 37:5 - Buku Lopatulika

5 Pereka njira yako kwa Yehova; khulupiriranso Iye, adzachichita.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Pereka njira yako kwa Yehova; khulupiriranso Iye, adzachichita.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Udzipereke m'manja mwa Chauta, umukhulupirire ndipo Iye adzakusamalira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Pereka njira yako kwa Yehova; dalira Iye ndipo Iyeyo adzachita izi:

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 37:5
14 Mawu Ofanana  

Ndipo anati, Yehova, Mulungu wa mbuyanga Abrahamu mundiyendetse ine bwino lero lino, mumchitire ufulu mbuyanga Abrahamu.


Ukatsimikiza mtima kakuti, kadzakhazikikira iwe; ndi kuunika kudzawala panjira zako.


Adadzitengera kwa Yehova; kuti adzampulumutsa, amlanditse tsopano popeza akondwera naye.


Umsenze Yehova nkhawa zako, ndipo Iye adzakugwiriziza, nthawi zonse sadzalola wolungama agwedezeke.


Pereka zochita zako kwa Yehova, ndipo zolingalira zako zidzakhazikika.


Pakuti zonsezi ndinazisunga mumtima ndikalondoletu zonsezi; kuti olungama ndi anzeru ndi ntchito zao ali m'manja a Mulungu; ngakhale kukonda ngakhale kudana anthu sadziwa; zonse zili m'tsogolo mwao.


Ndani anganene, chonena chake ndi kuchitikadi, ngati Ambuye salamulira?


Chifukwa chake ndinena kwa inu, Musadere nkhawa moyo wanu, chimene mudzadya ndi chimene mudzamwa; kapena thupi lanu, chimene mudzavala. Kodi moyo suli woposa chakudya, ndi thupi loposa chovala?


Ndipo Iye anati kwa ophunzira ake, Chifukwa chake ndinena ndinu, Musade nkhawa ndi moyo wanu, chimene mudzadya; kapena ndi thupi lanu, chimene mudzavala.


Mukadanena inu, Akalola Ambuye, ndipo tikakhala ndi moyo, tidzachita kakutikakuti.


ndi kutaya pa Iye nkhawa yanu yonse, pakuti Iye asamalira inu.


Ndipo iwo anati, Simunatinyenge, kapena kutisautsa, kapena kulandira kanthu m'manja mwa wina aliyense.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa