Masalimo 37:5 - Buku Lopatulika5 Pereka njira yako kwa Yehova; khulupiriranso Iye, adzachichita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pereka njira yako kwa Yehova; khulupiriranso Iye, adzachichita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Udzipereke m'manja mwa Chauta, umukhulupirire ndipo Iye adzakusamalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pereka njira yako kwa Yehova; dalira Iye ndipo Iyeyo adzachita izi: Onani mutuwo |