Masalimo 37:3 - Buku Lopatulika3 Khulupirira Yehova, ndipo chita chokoma; khala m'dziko, ndipo tsata choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Khulupirira Yehova, ndipo chita chokoma; khala m'dziko, ndipo tsata choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Khulupirira Chauta ndipo uzichita zabwino. Khala m'dziko ndi kutsata zokhulupirika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Khulupirira Yehova ndipo uzichita zabwino; khazikika mʼdziko ndi kutsata zokhulupirika. Onani mutuwo |
Chifukwa chake mbuye wanga mfumu amvere mau a kapolo wake. Ngati ndi Yehova anakuutsirani inu kutsutsana ndi ine, alandire chopereka; koma ngati ndi ana a anthu, atembereredwe pamaso pa Yehova, pakuti anandipirikitsa lero kuti ndisalandireko cholowa cha Yehova, ndi kuti, Muka, utumikire milungu ina.