Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 37:2 - Buku Lopatulika

2 Pakuti adzawamweta msanga monga udzu, ndipo adzafota monga msipu wauwisi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Pakuti adzawamweta msanga monga udzu, ndipo adzafota monga msipu wauwisi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 pakuti mosachedwa amanyala ngati udzu, ndipo amafota ngati masamba aaŵisi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 pakuti monga udzu iwo adzafota msanga, ngati mbewu zobiriwira adzanyala msanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 37:2
11 Mawu Ofanana  

Atuluka ngati duwa, nafota; athawa ngati mthunzi, osakhalitsa.


chakuti pophuka oipa ngati msipu, ndi popindula ochita zopanda pake; chitero kuti adzaonongeke kosatha.


Koma Inu, Yehova, muli m'mwamba kunthawi yonse.


Pakuti woipayo sadzalandira mphotho; nyali ya amphulupulu idzazima.


Popeza, Anthu onse akunga udzu, ndi ulemerero wao wonse ngati duwa la udzu. Udzuwo ungofota, ndi duwa lake lingogwa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa