Masalimo 37:1 - Buku Lopatulika1 Usavutike mtima chifukwa cha ochita zoipa, usachite nsanje chifukwa cha ochita chosalungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Usavutike mtima chifukwa cha ochita zoipa, usachite nsanje chifukwa cha ochita chosalungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Usamavutika ndi anthu oipa. Usamakhumbira kukhala ngati ochita zoipa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Usamavutike chifukwa cha anthu oyipa kapena kuchitira nsanje amene akuchita cholakwa; Onani mutuwo |