Masalimo 36:12 - Buku Lopatulika12 Pomwepo padagwera ochita zopanda pake. Anawalikha, ndipo sadzatha kuukanso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pomwepo padagwera ochita zopanda pake. Anawalikha, ndipo sadzatha kuukanso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Onani, ochita zoipa ali ngundangunda. Inu mwaŵagwetsa pansi ndipo sangathe kudzuka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Onani momwe ochita zoyipa agonera atagwa, aponyeni pansi, kuti asathe kudzukanso! Onani mutuwo |