Masalimo 34:3 - Buku Lopatulika3 Bukitsani pamodzi ndine ukulu wa Yehova, ndipo tikweze dzina lake pamodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Bukitsani pamodzi ndine ukulu wa Yehova, ndipo tikweze dzina lake pamodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Lalikani pamodzi nane ukulu wa Chauta, tiyeni limodzi tiyamike dzina lake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Lemekezani Yehova pamodzi ndi ine; tiyeni pamodzi tikuze dzina lake. Onani mutuwo |