Masalimo 33:8 - Buku Lopatulika8 Dziko lonse lapansi liope Yehova, ponse pali anthu achite mantha chifukwa cha Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Dziko lonse lapansi liope Yehova, ponse pali anthu achite mantha chifukwa cha Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Dziko lonse lapansi liwope Chauta. Anthu onse okhala pa dziko lapansi achite naye mantha, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Dziko lonse lapansi liope Yehova; anthu onse amulemekeze Iye. Onani mutuwo |