Masalimo 33:7 - Buku Lopatulika7 Amaunjika madzi a m'nyanja monga mulu, amakundika zakudya mosungiramo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Amaunjika madzi a m'nyanja monga mulu, amakundika zakuya mosungiramo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adasonkhanitsa pamodzi madzi a m'nyanja zakuya ndipo adaziikira malire kuti zisasefukire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iye amasonkhanitsa pamodzi madzi a mʼnyanja mʼmitsuko; amayika zozama mʼnyumba zosungiramo. Onani mutuwo |