Masalimo 33:6 - Buku Lopatulika6 Zakumwamba zinalengedwa ndi mau a Yehova; ndipo ndi mpweya wa m'kamwa mwake khamu lao lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Zakumwamba zinalengedwa ndi mau a Yehova; ndipo ndi mpweya wa m'kamwa mwake khamu lao lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Chauta adalankhula ndipo zakumwamba zidalengedwa. Zonse zakumeneko zidalengedwa pamene Iye adalankhula mau ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndi mawu a Yehova mayiko akumwamba anapangidwa, zolengedwa zake ndi mpweya wa mʼkamwa mwake. Onani mutuwo |