Masalimo 32:4 - Buku Lopatulika4 Chifukwa usana ndi usiku dzanja lanu linandilemera ine; uwisi wanga unasandulika kuuma kwa malimwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Chifukwa usana ndi usiku dzanja lanu linandilemera ine; uwisi wanga unasandulika kuuma kwa malimwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pakuti usana ndi usiku dzanja lanu lidandipsinja, motero nyonga zanga zidatha, monga amafotera masamba ndi dzuŵa lachilimwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pakuti usana ndi usiku dzanja lanu linandipsinja; mphamvu zanga zinatha monga nthawi yotentha yachilimwe. Sela Onani mutuwo |