Masalimo 32:3 - Buku Lopatulika3 Pamene ndinakhala chete mafupa anga anakalamba ndi kubuula kwanga tsiku lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pamene ndinakhala chete mafupa anga anakalamba ndi kubuula kwanga tsiku lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pamene ndinali ndisanaulule tchimo langa, thupi langa linali lofooka, chifukwa cha kubuula tsiku lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamene ndinali chete, mafupa anga anakalamba chifukwa cha kubuwula kwanga tsiku lonse. Onani mutuwo |