Masalimo 30:7 - Buku Lopatulika7 Inu, Yehova, munakhazikitsa phiri langa ndi kuyanja kwanu; munabisa nkhope yanu; ndinaopa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Inu, Yehova, munakhazikitsa phiri langa ndi kuyanja kwanu; munabisa nkhope yanu; ndinaopa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Chifukwa cha kukoma mtima kwanu, Inu Chauta, mudandikhazikitsa ngati phiri lolimba. Koma pamene mudandimana madalitso anu, ine ndidataya mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Inu Yehova, pamene munandikomera mtima, munachititsa phiri langa kuyima chilili; koma pamene munabisa nkhope yanu, ndinataya mtima. Onani mutuwo |