Masalimo 30:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo ine, ndinanena m'phindu langa, sindidzagwedezeka nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo ine, ndinanena m'phindu langa, sindidzagwedezeka nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma ine, pamene zinthu zidaandiyendera bwino, ndidati, “Sindidzagwedezeka konse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pamene ndinaona kuti ndili otetezedwa ndinati, “Sindidzagwedezekanso.” Onani mutuwo |