Masalimo 30:1 - Buku Lopatulika1 Ndidzakukwezani, Yehova; pakuti mwandinyamutsa, ndipo simunandikondwetsere adani anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndidzakukwezani, Yehova; pakuti mwandinyamutsa, ndipo simunandikondwetsera adani anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndidzakutamandani, Inu Chauta, pakuti mwanditulutsa m'dzenje la imfa. Simudalole kuti adani anga akondwere poona kuti ndikuvutika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndidzakukwezani Yehova, chifukwa mwanditulutsa kwakuya, ndipo simunalole kuti adani anga akondwere pa ine. Onani mutuwo |