Masalimo 29:11 - Buku Lopatulika11 Yehova adzapatsa anthu ake mphamvu, Yehova adzadalitsa anthu ake ndi mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Yehova adzapatsa anthu ake mphamvu, Yehova adzadalitsa anthu ake ndi mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta amapatsa anthu ake mphamvu. Amaŵadalitsa anthu ndi mtendere. Salmo la Davide. Nyimbo yoimba potsekula Nyumba ya Mulungu Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehova amapereka mphamvu kwa anthu ake; Yehova amadalitsa anthu ake ndi mtendere. Onani mutuwo |