Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 29:9 - Buku Lopatulika

9 Liu la Yehova liswetsa nyama zazikazi, ndipo lipulula nkhalango; ndipo mu Kachisi mwake zonse zili m'mwemo zimati, Ulemerero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Liu la Yehova liswetsa nyama zazikazi, ndipo lipulula nkhalango; ndipo m'Kachisi mwake zonse zili m'mwemo zimati, Ulemerero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Liwu la Chauta likuzunguza miŵanga likupulula masamba a mitengo yonse m'dondo. Onse a m'nyumba mwake akufuula kuti, “Ulemererowo!”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Liwu la Yehova limapindapinda mibawa ndi kuyeretsa nkhalango. Ndipo mʼNyumba mwake onse amafuwula kuti, “Ulemerero!”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 29:9
10 Mawu Ofanana  

Yehova, ndikonda chikhalidwe cha nyumba yanu, ndi malo akukhalamo ulemerero wanu.


Tidalingalira zachifundo chanu, Mulungu, m'kati mwa Kachisi wanu.


Kuti ndione mphamvu yanu ndi ulemerero wanu, monga ndinakuonani m'malo oyera.


Pakuti kuchimwa kwayaka ngati moto kumaliza lunguzi ndi minga, inde kuyaka m'nkhalango ya m'thengo, ndipo zifuka chapamwamba, m'mitambo yautsi yochindikira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa