Masalimo 29:10 - Buku Lopatulika10 Yehova anakhala pa chigumula, inde Yehova akhala mfumu kunthawi yonka muyaya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Yehova anakhala pa chigumula, inde Yehova akhala mfumu kunthawi yonka muyaya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chauta amalamulira nyanja zonse, amakhala kwamuyaya pa mpando wake wachifumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Yehova amakhala pamwamba pa madzi osefukira, Yehova ndiye mfumu kwamuyaya. Onani mutuwo |