Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 29:10 - Buku Lopatulika

10 Yehova anakhala pa chigumula, inde Yehova akhala mfumu kunthawi yonka muyaya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Yehova anakhala pa chigumula, inde Yehova akhala mfumu kunthawi yonka muyaya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Chauta amalamulira nyanja zonse, amakhala kwamuyaya pa mpando wake wachifumu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Yehova amakhala pamwamba pa madzi osefukira, Yehova ndiye mfumu kwamuyaya.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 29:10
16 Mawu Ofanana  

Ndine, taonani, ndipo Ine ndidzadzetsa chigumula cha madzi padziko lapansi, kuti chiononge zamoyo zonse, m'mene muli mpweya wa moyo pansi pathambo; zinthu zonse za m'dziko lapansi zidzafa.


Ndani anachikumbira mchera chimvula, kapena njira ya bingu la mphezi,


Yehova ndiye Mfumu kunthawi yamuyaya; aonongeka amitundu m'dziko lake.


Liu la Yehova lili pamadzi; Mulungu wa ulemerero agunda, ndiye Yehova pamadzi ambiri.


Amene atontholetsa kukuntha kwa nyanja, kukuntha kwa mafunde ake, ndi phokoso la mitundu ya anthu.


Ndipo Iyeyu adzaweruza dziko lapansi m'chilungamo, nadzaweruza anthu molunjika.


Yehova achita ufumu; wadziveka ndi ukulu; wadziveka Yehova, wadzimangirira mphamvu m'chuuno; dziko lomwe lokhalamo anthu likhakizika, silidzagwedezeka.


Yehova ndiye mfumu; mitundu ya anthu injenjemere; Iye akhala pakati pa akerubi; dziko lapansi ligwedezeke.


Ndipo masiku a mafumu aja Mulungu wa Kumwamba adzaika ufumu woti sudzaonongeka kunthawi zonse, ndi ulamuliro wake sudzasiyidwira mtundu wina wa anthu, koma udzaphwanya ndi kutha maufumu ao onse, nudzakhala chikhalire.


Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo.


Ndipo iwo anachita mantha aakulu, nanenana wina ndi mnzake, Uyu ndani nanga, kuti ingakhale mphepo ndi nyanja zimvera Iye?


Ndipo kwa Mfumu yosatha, yosavunda, yosaoneka, Mulungu wa yekha, ukhale ulemu ndi ulemerero, kufikira nthawi za nthawi. Amen.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa