Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 29:8 - Buku Lopatulika

8 Liu la Yehova ligwedeza chipululu; Yehova agwedeza chipululu cha Kadesi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Liu la Yehova ligwedeza chipululu; Yehova agwedeza chipululu cha Kadesi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Liwu la Chauta likugwedeza chipululu, Chauta akugwedeza chipululu cha Kadesi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Liwu la Yehova limagwedeza chipululu; Yehova amagwedeza chipululu cha Kadesi.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 29:8
9 Mawu Ofanana  

Amene agwedeza dziko lapansi lichoke m'malo mwake, ndi mizati yake injenjemere.


Pamenepo linagwedezeka, ndi kutenthemera dziko lapansi, ndi maziko a mapiri ananjenjemera nagwedezeka, pakuti anakwiya Iyeyo.


Chinkana madzi ake akokoma, nachita thovu, nagwedezeka mapiri ndi kudzala kwake.


Chifukwa chake ndidzanthunthumiritsa miyamba, ndipo dziko lapansi lidzagwedezeka kuchokera m'malo ake, m'mkwiyo wa Yehova wa makamu, tsiku la mkwiyo wake waukali.


Ndipo Yehova adzadzuma ali ku Ziyoni, ndi kumveketsa mau ake ali ku Yerusalemu; ndi thambo ndi dziko lapansi zidzagwedezeka; koma Yehova adzakhala chopulumukirako anthu adzakhala chopulumukirako anthu ake, ndi linga la ana a Israele.


Nena ndi Zerubabele chiwanga cha Yuda, kuti, Ndidzagwedeza miyamba ndi dziko lapansi;


Pakuti atero Yehova wa makamu: Kamodzinso, katsala kanthawi, ndidzagwedeza miyamba ndi dziko lapansi, ndi nyanja, ndi mtunda womwe;


Ndipo anamuka, nadza kwa Mose, ndi Aroni, ndi khamu lonse la ana a Israele, ku chipululu cha Parani ku Kadesi; ndipo anabwezera mau iwowa, ndi khamu lonse, nawaonetsa zipatso za dzikoli.


amene mau ake anagwedeza dziko pamenepo; koma tsopano adalonjeza, ndi kuti, Kamodzinso ndidzagwedeza, si dziko lokha, komanso m'mwamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa