Masalimo 28:2 - Buku Lopatulika2 Mverani mau a kupemba kwanga, pamene ndilirira Inu, pamene ndikweza manja anga kuloza ponenera panu poyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mverani mau a kupemba kwanga, pamene ndilirira Inu, pamene ndikweza manja anga kuloza ponenera panu poyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Imvani kupempha kwanga, pamene ndikulirira Inu kuti mundithandize, pamene ndikukupembedzani pokweza manja anga ku malo anu opatulika kopambana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Imvani kupempha chifundo kwanga pomwe ndikuyitana kwa Inu kuti mundithandize, pomwe ndikukweza manja anga kuloza ku malo anu oyeretsetsa. Onani mutuwo |