Masalimo 25:2 - Buku Lopatulika2 Mulungu wanga, ndakhulupirira Inu, ndisachite manyazi; adani anga asandiseke ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mulungu wanga, ndakhulupirira Inu, ndisachite manyazi; adani anga asandiseke ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndikuika mtima wanga pa Inu Mulungu wanga. Musalole kuti adani anga andichititse manyazi, musalole kuti akondwere pamene ine ndikuvutika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndimadalira Inu Mulungu wanga. Musalole kuti ndichite manyazi kapena kuti adani anga andipambane. Onani mutuwo |