Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 25:1 - Buku Lopatulika

1 Ndikweza moyo wanga kwa Inu, Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndikweza moyo wanga kwa Inu, Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Ndikupereka mtima wanga kwa Inu Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Kwa Inu Yehova, ndipereka moyo wanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 25:1
5 Mawu Ofanana  

Mundimvetse chifundo chanu mamawa; popeza ndikhulupirira Inu: Mundidziwitse njira ndiyendemo; popeza ndikweza moyo wanga kwa Inu.


Woyera m'manja, ndi woona m'mtima, ndiye; iye amene sanakweze moyo wake kutsata zachabe, ndipo salumbira monyenga.


Kondwetsani moyo wa mtumiki wanu; pakuti ndikwezera moyo wanga kwa Inu, Ambuye.


Titukulire mitima yathu ndi manja athu omwe kwa Mulungu ali kumwamba.


Ndipo Hana anayankha, nati, Iai, mbuyanga. Ine ndili mkazi wa mtima wachisoni; sindinamwe vinyo kapena chakumwa chowawa, koma ndinatsanulira mtima wanga pamaso pa Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa