Masalimo 23:6 - Buku Lopatulika6 Inde ukoma ndi chifundo zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala m'nyumba ya Yehova masiku onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Inde ukoma ndi chifundo zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala m'nyumba ya Yehova masiku onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Zoonadi, zokoma zanu ndi chikondi chanu zidzakhala ndi ine masiku onse a moyo wanga. Ndidzakhala m'Nyumba mwanu moyo wanga wonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova kwamuyaya. Onani mutuwo |