Masalimo 23:5 - Buku Lopatulika5 Mundiyalikira gome pamaso panga m'kuona kwa adani anga; mwandidzoza mutu wanga mafuta; chikho changa chisefuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mundiyalikira gome pamaso panga m'kuona kwa adani anga; mwandidzoza mutu wanga mafuta; chikho changa chisefuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Inu mumandikonzera chakudya, adani anga akuwona. Mumandilandira bwino podzoza mutu wanga ndi mafuta, mumadzaza chikho changa mpaka kusefukira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mumandikonzera chakudya adani anga akuona. Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta; chikho changa chimasefukira. Onani mutuwo |