Masalimo 23:3 - Buku Lopatulika3 Atsitsimutsa moyo wanga; anditsogolera m'mabande a chilungamo, chifukwa cha dzina lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Atsitsimutsa moyo wanga; anditsogolera m'mabande a chilungamo, chifukwa cha dzina lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Amatsitsimutsa moyo wanga. Amanditsogolera m'njira za chilungamo malinga ndi ulemerero wa dzina lake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 amatsitsimutsa moyo wanga. Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo chifukwa cha dzina lake. Onani mutuwo |