Masalimo 23:2 - Buku Lopatulika2 Andigonetsa kubusa lamsipu, anditsogolera kumadzi odikha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Andigonetsa kubusa lamsipu, anditsogolera kumadzi odikha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Amandigoneka pa busa lamsipu. Amanditsogolera ku madzi odikha kokapumulirako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Amandigoneka pa msipu wobiriwira, amanditsogolera ku madzi akumwa abwino, Onani mutuwo |