Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 22:9 - Buku Lopatulika

9 Pakuti Inu ndinu wondibadwitsa; wondikhulupiritsa pokhala ine pa bere la mai wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Pakuti Inu ndinu wondibadwitsa; wondikhulupiritsa pokhala ine pa bere la mai wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Komabe Inu ndinu amene mudalola kuti ndibadwe. Inu ndinu chikhulupiriro changa, mudandilera bwino ndili mwana woyamwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Komabe Inu ndinu amene munandibadwitsa, munanditulutsa mʼmimba mwa amayi anga. Munachititsa kuti ndizikudalirani ngakhale pa nthawi imene ndinkayamwa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 22:9
8 Mawu Ofanana  

Mulungu, mwandiphunzitsa kuyambira ubwana wanga; ndipo kufikira lero ndilalikira zodabwitsa zanu.


Inu munandigwiriziza kuyambira ndisanabadwe, kuyambira pa thupi la mai wanga wondichitira zokoma ndinu; ndidzakulemekezani kosalekeza.


Pakuti kwa ife mwana wakhanda wabadwa, kwa ife mwana wamwamuna wapatsidwa; ndipo ulamuliro udzakhala pa phewa lake, ndipo adzamutcha dzina lake Wodabwitsa, Wauphungu, Mulungu wamphamvu, Atate Wosatha, Kalonga wa mtendere.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa