Masalimo 22:29 - Buku Lopatulika29 Onenepa onse a padziko lapansi adzadya nadzagwadira; onse akutsikira kufumbi adzawerama pamaso pake, ndi iye amene sadziwa kusunga moyo wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Onenepa onse a pa dziko lapansi adzadya nadzagwadira; onse akutsikira kufumbi adzawerama pamaso pake, ndi iye amene sadziwa kusunga moyo wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Anthu onse odzitama adzamuŵeramira. Anthu onse oloŵa m'manda nawonso adzamugwadira, ndiye kuti onse osatha kudzisungira moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Anthu olemera onse a dziko lapansi adzachita phwando ndi kulambira; onse amene amapita ku fumbi adzagwada pamaso pake; iwo amene sangathe kudzisunga okha ndi moyo. Onani mutuwo |