Masalimo 22:28 - Buku Lopatulika28 Pakuti ufumuwo ngwa Yehova; Iye achita ufumu mwa amitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Pakuti ufumuwo ngwa Yehova; Iye achita ufumu mwa amitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Pakuti ulamuliro ndi wake wa Chauta, Iye amalamula anthu a mitundu yonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 pakuti ulamuliro ndi wake wa Yehova ndipo Iye amalamulira anthu a mitundu yonse. Onani mutuwo |