Masalimo 22:26 - Buku Lopatulika26 Ozunzika adzadya nadzakhuta, adzayamika Yehova iwo amene amfuna, ukhale moyo mtima wako nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ozunzika adzadya nadzakhuta, adzayamika Yehova iwo amene amfuna, ukhale moyo mtima wako nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Ozunzika adzadya ndi kukhuta, ofunafuna Chauta adzamtamanda. Ine ndidzati, “Mitima yanu ikhale ndi moyo nthaŵi zonse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Osauka adzadya ndipo adzakhuta; iwo amene amafunafuna Yehova adzamutamanda. Mitima yanu ikhale ndi moyo mpaka muyaya! Onani mutuwo |