Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 22:25 - Buku Lopatulika

25 Lemekezo langa lidzakhala la Inu mu msonkhano waukulu, zowinda zanga ndidzazichita pamaso pa iwo akumuopa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Lemekezo langa lidzakhala la Inu mu msonkhano waukulu, zowinda zanga ndidzazichita pamaso pa iwo akumuopa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Ndidzakutamandani pa msonkhano waukulu chifukwa cha zimene mwandichitira. Zimene ndidalonjeza ndidzazichita pamaso pa onse okumverani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Ndidzakutamandani pa msonkhano waukulu chifukwa cha zimene mwandichitira. Ndidzakwaniritsa lonjezo langa pamaso pa amene amaopa Inu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 22:25
11 Mawu Ofanana  

Aleluya. Ndidzayamika Yehova ndi mtima wonse, mu upo wa oongoka mtima, ndi mumsonkhano.


Ndidzalalikira dzina lanu kwa abale anga, pakati pa msonkhano ndidzakulemekezani.


Ndidzakuyamikani mu msonkhano waukulu; m'chikhamu cha anthu ndidzakulemekezani.


Zowindira Inu Mulungu, zili pa ine, ndidzakuchitirani zoyamika.


Mu Ziyoni akulemekezani Inu mwachete, Mulungu, adzakuchitirani Inu chowindachi.


Ndidzalowa m'nyumba yanu ndi nsembe zopsereza, ndidzakuchitirani zowinda zanga,


Idzani, imvani, inu nonse akuopa Mulungu, ndipo ndidzafotokozera zonse anazichitira moyo wanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa