Masalimo 22:24 - Buku Lopatulika24 Pakuti sanapeputse ndipo sananyansidwe ndi zunzo la wozunzika; ndipo sanambisire nkhope yake; koma pomfuulira Iye, anamva. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Pakuti sanapeputsa ndipo sananyansidwe ndi zunzo la wozunzika; ndipo sanambisire nkhope yake; koma pomfuulira Iye, anamva. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 “Pakuti sadanyoze munthu wozunzika, sadaipidwe ndi masautso ake, sadamubisire nkhope yake, koma adamumvera pamene adamdandaulira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Pakuti Iye sanapeputse kapena kunyoza kuvutika kwa wosautsidwayo; Iye sanabise nkhope yake kwa iye. Koma anamvera kulira kwake kofuna thandizo. Onani mutuwo |