Masalimo 22:27 - Buku Lopatulika27 Malekezero onse a dziko lapansi adzakumbukira nadzatembenukira kwa Yehova, ndipo mafuko onse a amitundu adzagwadira pamaso panu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Malekezero onse a dziko lapansi adzakumbukira nadzatembenukira kwa Yehova, ndipo mafuko onse a amitundu adzagwadira pamaso panu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Anthu a mitundu yonse pa dziko lapansi adzakumbukira nadzatembenukira kwa Chauta, mabanja a mitundu ina ya anthu adzampembedza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Malekezero onse a dziko lapansi adzakumbukira Yehova ndi kutembenukira kwa Iye, ndipo mabanja a mitundu ya anthu adzawerama pamaso pake, Onani mutuwo |