Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 19:10 - Buku Lopatulika

10 Ndizo zifunika koposa golide, inde, golide wambiri woyengetsa; zizuna koposa uchi ndi zakukha za zisa zake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndizo zifunika koposa golide, inde, golide wambiri woyengetsa; zizuna koposa uchi ndi zakukha za zisa zake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Zonsezi nzoyenera kuzikhumbira kupambana golide, ngakhale golide wambiri wamtengowapatali, nzotsekemera kupambana uchi, ngakhale uchi wozuna kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 ndi a mtengowapatali kuposa golide, kuposa golide weniweni; ndi otsekemera kuposa uchi, kuposa uchi wochokera pa chisa chake.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 19:10
13 Mawu Ofanana  

Sindinabwerera kusiya malamulo a pa milomo yake; ndasungitsa mau a pakamwa pake koposa lamulo langalanga.


Mau anu azunadi powalawa ine! Koposa uchi m'kamwa mwanga.


Chifukwa chake ndikonda malamulo anu koposa golide, inde golide woyengeka.


Chilamulo cha pakamwa panu chindikomera koposa golide ndi siliva zikwizikwi.


Mudzakhutitsa moyo wanga ngati ndi mafuta ndi zonona; ndipo pakamwa panga ndidzakulemekezani ndi milomo yakufuula mokondwera.


Kodi kulandira nzeru sikupambana ndi golide, kulandira luntha ndi kusankhika koposa siliva?


Mwananga, idya uchi pakuti ngwabwino, ndi chisa chake chitsekemera m'kamwa mwako.


Chipatso changa chiposa golide, ngakhale golide woyengeka; phindu langa liposa siliva wosankhika.


Ndipo ndinatenga kabuku m'dzanja la mngelo, ndipo ndinakadya; ndipo kanali m'kamwa mwanga kozuna ngati uchi; ndipo pamene ndinakadya m'mimba mwanga mudawawa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa