Masalimo 19:9 - Buku Lopatulika9 Kuopa Yehova kuli mbee, kwakukhalabe nthawi zonse; maweruzo a Yehova ali oona, alungama konsekonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Kuopa Yehova kuli mbee, kwakukhalabe nthawi zonse; maweruzo a Yehova ali oona, alungama konsekonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Kuwopa Chauta ndiye chinthu changwiro, chimakhala mpaka muyaya. Chiweruzo cha Chauta nchoona, ncholungama nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kuopa Yehova ndiye chinthu changwiro, chimakhala mpaka muyaya. Maweruzo a Yehova ndi owona ndipo onse ndi olungama; Onani mutuwo |