Masalimo 18:8 - Buku Lopatulika8 Unakwera utsi wotuluka m'mphuno mwake, ndi moto wa m'kamwa mwake unanyeka nuyakitsa makala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Unakwera utsi wotuluka m'mphuno mwake, ndi moto wa m'kamwa mwake unanyeka nuyakitsa makala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 M'mphuno mwake munkafuka utsi, m'kamwa mwake munkatuluka moto woononga, makala amoto anali laŵilaŵi kuchokera m'kamwa momwemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mʼmphuno mwake munatuluka utsi; moto wonyeketsa unatuluka mʼkamwa mwake, makala amoto anali lawilawi mʼkamwa mwake. Onani mutuwo |