Masalimo 18:43 - Buku Lopatulika43 Mwandipulumutsa pa zolimbana nane za anthu; mwandiika mutu wa amitundu; mtundu wa anthu sindinaudziwe udzanditumikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Mwandipulumutsa pa zolimbana nane za anthu; mwandiika mutu wa amitundu; mtundu wa anthu sindinaudziwa udzanditumikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Inu mudandipulumutsa kwa anthu olimbana nane, Inu mudandisandutsa mfumu ya mitundu yonse. Choncho anthu osaŵadziŵa ankanditumikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Inu mwandipulumutsa mʼmanja mwa anthu; mwandisandutsa kukhala mtsogoleri wa anthu a mitundu ina. Anthu amene sindikuwadziwa ali pansi pa ulamuliro wanga. Onani mutuwo |