Masalimo 18:42 - Buku Lopatulika42 Pamenepo ndinawapera ngati fumbi la kumphepo; ndinawakhuthula ngati matope a pabwalo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Pamenepo ndinawapera ngati fumbi la kumphepo; ndinawakhuthula ngati matope a pabwalo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Ndidaŵaperapera ngati fumbi louluka ndi mphepo. Ndimaŵapondereza ngati matope amumseu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Ine ndinawaperesa ngati fumbi lowuluka ndi mphepo. Ndinawapondaponda ngati matope a mʼmisewu. Onani mutuwo |